LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 145 tsa. 10
  • Kukonzeka Kukalalikila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukonzeka Kukalalikila
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Phunzilo 3
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Kudzipeleka na Mtima Wonse
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 145 tsa. 10

Nyimbo 145

Kukonzeka Kukalalikila

Yopulinta

(Yeremiya 1:17)

  1. N’kuseni,

    Tikonzeke

    Kupita mu‘tumiki.

    Mvula ikugwa,

    Ndipo kwazizila.

    Tingafune kupitiliza

    kugona.

    (KOLASI)

    Pemphelo na kukonzekela,

    Izi tikacita;

    Tidzalalikila Uthenga,

    Mosaleka.

    Angelo amatithandiza.

    Yesu awatuma.

    Na bwenzi lokhulupilika,

    Sitifoka.

  2. Cimwemwe

    Tidzapeza

    Ngati tipitiliza.

    Ndipo tidziŵa

    Kuti M’lungu wathu,

    Amaona zonse zimene

    ticita.

    (KOLASI)

    Pemphelo na kukonzekela,

    Izi tikacita;

    Tidzalalikila Uthenga,

    Mosaleka.

    Angelo amatithandiza.

    Yesu awatuma.

    Na bwenzi lokhulupilika,

    Sitifoka.

(Onaninso Mlal. 11:4; Mat. 10:5, 7; Luka 10:1; Tito 2:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani