LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mb phunzilo 3
  • Phunzilo 3

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilo 3
  • Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • ‘Ine Nilipo, N’tumizeni!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
mb phunzilo 3

Phunzilo 3

1 Petulo 3:8

Davide amva kuti mnzake wadwala.

Conco akamba kuti: “Nidziŵa zimene nidzacita.

Nidzamulembela kalata kuti nimulimbikitse, ndiyeno nidzamupelekela.”

Ukaonetsa kukoma mtima, mnzako adzakondwela.

ZOCITA

Muŵelengeleni mwana wanu:

1 Petulo 3:8

Uzani mwana wanu kuti aloze:

Nyumba Deski Davide

Dzuŵa Mbalame Mtengo

M’funseni mwana wanu:

Kodi udziŵako munthu wina amene adwala?

Tingamulimbikitse bwanji munthuyo?

[Cithunzi 8]

[Cithunzi 8]

[Cithunzi 9]

[Cithunzi 9]

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani