LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 90
  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kukongola kwa Imvi
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 90

Nyimbo 90

Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi

(Miyambo 16:31)

1. Pakati pathu pali

Achikulire.

Akukondabe M’lungu

Sanamusiye.

Ena imfa ya mnzawo

Ikuwawawa.

Tate atonthozeni,

N’kuwalimbitsa.

(KOLASI)

Mumakumbukira

Zochita zawo.

Tate auzeni:

“Mwachita bwino.”

2. Imvi za olungama

Ndi zokongola.

Zimasangalatsadi

Tate Yehova.

Ife tikumbukire

Pa nthawi ina

Pa unyamata wawo

Ankayesetsa.

(KOLASI)

Mumakumbukira

Zochita zawo.

Tate auzeni:

“Mwachita bwino.”

(Onaninso Sal. 71:9, 18; Miy. 20:29; Mat. 25:21, 23; Luka 22:28; 1 Tim. 5:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani