LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 112
  • Yehova, Mulungu Wamkulu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova, Mulungu Wamkulu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Wamkulu, Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 112

Nyimbo 112

Yehova, Mulungu Wamkulu

(Ekisodo 34:6, 7)

1. Inu Yehova M’lungu wamkulu

Ndinu woyeneradi

Kutamandidwa zedi.

Ndinu wabwino ndi wolungama.

Ndinu M’lungu kosatha.

2. Mumakhululukiradi anthu

Amene monga inu

Ndi achifundo ndithu.

Mumasonyeza kukoma mtima

Pa zonse mumachita.

3. Mutamandidwe ndi anthu onse

Dzina lanu liyere

Wina asalikane.

Dziko lapansi likhale mmene

Inu mumafunira.

(Onaninso Deut. 32:4; Miy. 16:12; Mat. 6:10; Chiv. 4:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani