LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 79
  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mphamvu ya Kukoma Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukoma Mtima Khalidwe Limene Limaonekela M’mawu na M’zocita
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Lolani Kuti “Lamulo la Kukoma Mtima Kosatha” Lizikutsogolelani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • “Bwelani kwa Ine . . . Ndipo Ndidzakutsitsimutsani”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 79

Nyimbo 79

Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri

(Aefeso 4:32)

1. Tikuthokoza chifukwa choti

Yehova tam’dziwa.

Ngakhale n’ngwanzeru ndi wamphamvu,

Iye ndi wokoma mtima.

2. Yesu akuitana otopa

Awatsitsimule.

Ndipo goli lake ndi lofewa

Chifukwa n’ngokoma mtima.

3. Mulungu komanso Mbuye Yesu

Tiziwatsanzira.

M’zochita zathu tifunikira

Kukhala okoma mtima.

(Onaninso Mika 6:8; Mat. 11:28-30; Akol. 3:12; 1 Pet. 2:3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani