LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 116
  • Mphamvu ya Kukoma Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mphamvu ya Kukoma Mtima
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri
    Imbirani Yehova
  • Kukoma Mtima Khalidwe Limene Limaonekela M’mawu na M’zocita
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Lolani Kuti “Lamulo la Kukoma Mtima Kosatha” Lizikutsogolelani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Tiziyamikila Kukoma Mtima Kwakukulu Kumene Tinalandila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 116

NYIMBO 116

Mphamvu ya Kukoma Mtima

Yopulinta

(Aefeso 4:32)

  1. 1. Tiyamikila imwe Yehova,

    M’lungu wacikondi.

    Ngakhale kuti muli na mphamvu

    Ndimwedi wokoma mtima.

  2. 2. Mwana wanu Yesu aitana

    Onse ovutika,

    Kuti iwo abwele kwa iye,

    Ndipo adzatonthozedwa.

  3. 3. Tikhale ngati M’lungu na Yesu,

    Mu zocita zathu.

    Ngati tikhala okoma mtima,

    Tidzakhaladi amphamvu.

(Onaninso Mika 6:8; Mat. 11:28-30; Akol. 3:12; 1 Pet. 2:3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani