LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 72
  • Tizisonyeza Chikondi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tizisonyeza Chikondi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kukulitsa Mkhalidwe wa Cikondi
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndiye Cikondi”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 72

Nyimbo 72

Tizisonyeza Chikondi

(1 Akorinto 13:1-8)

1. Tikupemphera kwa Mulungu,

Kuti tizikonda anzathu.

Tikakhala ndi mzimu wake

Ndiye kuti tingakondane.

Tingakhale ndi luso, nzeru,

Komabe osakonda anthu.

Izi sizingatithandize.

Choncho chikondi tikulitse.

2. Tisadalire nzeru zokha

Pamene tiphunzitsa nkhosa.

Ndi kofunika kuzikonda

Kuti cho’nadi chizilowa.

Ngakhale tikalakwiridwa

Tidzakhalabe opirira.

Chikondi chipirira zonse

Ndiponso sichidzatha konse.

(Onaninso Yoh. 21:17; 1 Akor. 13:13; Agal. 6:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani