LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 80
  • Tizichita Zinthu Zabwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tizichita Zinthu Zabwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ubwino
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ubwino—Kodi tingalikulitse bwanji khalidwe limeneli?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • ‘Laŵani’ Ubwino wa Yehova—Motani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Imbirani Yehova
sn nyimbo 80

Nyimbo 80

Tizichita Zinthu Zabwino

(Salimo 119:66)

1. N’zosangalatsa kudziwa

Ubwino wa Yehova.

Monga Tate wakumwamba

Amachita zabwino.

Amasonyeza chifundo

Ndipo amatikonda.

N’ngoyenera kum’lambira

Ndi kumutumikira.

2. M’chifaniziro cha M’lungu

Anatilenga ife,

Kuti makhalidwe ake

Inde, tiwasonyeze.

Ubwino wathu ukule

Mulungu tim’tsanzire,

Chipatso cha mzimu wake

Tifuna tisonyeze.

3. Makamaka ’bale athu

Tiwakomere mtima,

Komanso kwa anthu onse

Tisonyeze ubwino.

Pomwe tikulalikira

Uthenga wa Ufumu

Tikhale opanda tsankho

Abwino m’zinthu zonse.

(Onaninso Sal. 103:10; Maliko 10:18; Agal. 5:22; Aef. 5:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani