LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 132
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Nyimbo ya Cipambano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 132

Nyimbo 132

Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

(Ekisodo 15:1)

1. Muimbireni Yehova M’lungu wokwezeka.

Anaponya m’nyanja Aigup’to onyada.

Tamandani Ya. Palibe wina womuposa.

Yehova ndi dzina lake. Ndi wopambana.

(KOLASI)

Yehova ndinu wokwezeka

Simunasinthe ndinube Mfumu.

Adani anu muwagonjetsa

N’kuyeretsa dzina lanu.

2. Mitundu yonse eti ikutsutsa Yehova.

Iwonongedwabe ngakhale ndi yamphamvu.

Posachedwapa isesedwa ndi Amagedo.

Idzadziwa kuti Yehova ndi Mulungu.

(KOLASI)

Yehova ndinu wokwezeka

Simunasinthe ndinube Mfumu.

Adani anu muwagonjetsa

N’kuyeretsa dzina lanu.

(Onaninso Sal. 2:2, 9; 92:8; Mal. 3:6; Chiv. 16:16.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani