LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 30
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 30

Nyimbo 30

Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira

(Chivumbulutso 11:15)

1. Tsikuli n’lapadera. M’lungu akulamula.

Waikatu mwala mu Ziyoni.

Onse akweze mawu. Aimbire Mulungu.

Khristu Mpulumutsi wakhala pampando.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

2. Khristu ali pampando, Nkhondo yayandikira.

Dongosolo la Satana litha.

Ndi nthawi yolalika kwa anthu ochuluka.

Nyengo yoti ofatsa asankhe M’lungu.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

3. Tidalira Mfumuyo. Ndi yochititsa chidwi.

Ibwera mu dzina la Yehova.

Tilowe mukachisi, Tim’pembedze Mulungu.

Posachedwa adzalamulira zonse.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

(Onaninso 2 Sam. 7:22; Dan. 2:44; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani