LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 21
  • Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 21

NYIMBO 21

Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba

Yopulinta

(Mateyu 6:33)

  1. 1. Yehova asangalala,

    Na Ufumu wa Khristu.

    Adzaugwilitsa nchito,

    Kukonza zinthu zonse.

    (KOLASI)

    M’fune Ufumu coyamba,

    Na cilungamo cake.

    Tumikilani Yehova

    Ndipo mutamandeni.

  2. 2. M’fune Ufumu coyamba,

    M’malo modela nkhawa.

    Kuti maŵa tidya ciani,

    Dalilani Yehova.

    (KOLASI)

    M’fune Ufumu coyamba,

    Na cilungamo cake.

    Tumikilani Yehova

    Ndipo mutamandeni.

  3. 3. Lalikilani uthenga;

    Onse adziŵe kuti,

    Adzapeza madalitso

    Mu Ufumu wa M’lungu.

    (KOLASI)

    M’fune Ufumu coyamba,

    Na cilungamo cake.

    Tumikilani Yehova

    Ndipo mutamandeni.

(Onaninso Sal. 27:14; Mat. 6:34; 10:11, 13; 1 Pet. 1:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani