LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 28
  • Nyimbo Yatsopano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nyimbo Yatsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 28

Nyimbo 28

Nyimbo Yatsopano

(Salmo 98)

1. Imbira M’lungu, Imba nyimbo yatsopano;

Unene kwa onse Ntchito zake zonse.

Umutamande, Mulungu ndi wopambana.

Poweruza anthu N’ngwachilungamodi.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

2. Fu’la mokondwa, Fuula kwa Mfumu yathu!

Mutamandenitu, Ndi nyimbo mokondwa.

Tiyeni tonse Timuimbire mokweza.

Zeze ndi lipenga Ziimbe pamodzi.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

3. Nyanja ndi zinthu Za momwemo zim’tamande.

Inde chilengedwe Chonse chim’tamande.

Mtunda ukondwe, Mitsinjenso ikondwere.

Mapiri ndi zigwa, Nazo zim’tamande.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

(Onaninso Sal. 96:1; 149:1; Yes. 42:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani