LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 105
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Zakumwamba Zilengeza Ulemelelo wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cilengedwe Citamanda Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 105

Nyimbo 105

Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu

(Salimo 19)

1. Kumwamba kumatamanda Yehova.

Ntchito za manja ’ke Timazionatu.

Nthawi zonse zimamutamanda,

Nyenyezi zimasonyeza Kuti ndi wamphamvu.

2. Malamulo a M’lungu ndi angwiro,

Zikumbutso zake Zimatetezadi.

Zigamulo zake n’zolondola.

Mawu ake n’ngolungama. N’ngokoma kwambiri.

3. Kuopa Mulungu ndi kwamuyaya.

Malamulo ake Aposa golide.

Iwotu amatitsogolera.

Dzina lake loyeralo Tililemekeze.

(Onaninso Sal. 111:9; 145:5; Chiv. 4:11)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani