LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 124
  • Alandireni Bwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Alandireni Bwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Alandileni na Manja Aŵili
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kucelezana ni Khalidwe Lofunika Kwambili
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Gaŵanani ndi Ena “Zabwino” mwa Kukhala Woceleza (Mat. 12:35a)
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 124

Nyimbo 124

Alandireni Bwino

(Machitidwe 17:7)

1. Yehova ndi M’lungu wopanda tsankho

Amapatsa onse zofuna zawo.

Amapatsa dzuwa

Ngakhalenso mvula

Amatisangalatsa mtima.

Osauka tikamawathandiza.

Mulungu wathu tidzamutsanzira,

Adzatidalitsa tikamachitira

Ena zinthu mokoma mtima.

2. Pothandiza ena sitingadziwe

Madalitso omwe tingalandire.

Angakhale anthu achilendo ndithu,

Tiwapatse zosowa zawo.

Monga Lidiya wa m’nthawi yakale,

Akabwera kwathu tiwalandire.

M’lungu amadziwa

onse om’tsanzira

Pochitira ena chifundo.

(Onaninso Mac. 16:14, 15; Aroma 12:13; 1 Tim. 3:2; Aheb. 13:2; 1 Pet. 4:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani