LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • ll gao 10 masa. 22-23
  • Kodi Amene Amamvetsela kwa Mulungu Adzapeza Madalitso Abwanji?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Amene Amamvetsela kwa Mulungu Adzapeza Madalitso Abwanji?
  • Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Nkhani Zofanana
  • Gao 10
    Mvetselani kwa Mulungu
  • “Taonani! Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga N’zatsopano”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Anzake A Mulungu Adzakhala mu Paladaiso
    Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
  • Ufumu Umene Udzalamulila Dziko Lonse
    Phunzitsani Ana Anu
Onaninso Zina
Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
ll gao 10 masa. 22-23

GAO 10

Kodi Amene Amamvetsela kwa Mulungu Adzapeza Madalitso Abwanji?

Ambili amene anafa adzauka ndi kukhala ndi moyo padziko lapansi. Machitidwe 24:15

Anthu m’Paladaiso akulandila oukitsidwa

Taonani madalitso amene mudzalandila mtsogolo ngati mumvetsela kwa Yehova. Mudzakhala ndi thanzi labwino; sikudzakhala munthu wodwala kapena wofooka. Sikudzakhala anthu oipa ndipo mudzakhulupilila munthu aliyense.

Sikudzakhala zoŵaŵa, cisoni kapena kulila. Sikudzakhala kukalamba ndi kufa.

Anthu amene mudzakhala nao adzakhala anzanu ndi acibanja. Umoyo m’Paladaiso udzakhala wokondweletsa.

Sikudzakhala mantha. Anthu adzakhala okondwela kwambili.

Ufumu wa Mulungu udzatsiliza mavuto onse. Chivumbulutso 21:3, 4

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani