LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mb phunzilo 5
  • Phunzilo 5

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilo 5
  • Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tikuyamikani Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Makolo—Thandizani Ana Anu Kulimbitsa Cikhulupililo Cawo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
mb phunzilo 5

Phunzilo 5

1 Atesalonika 5:18

Ngati mnzako akupatsa mphatso kapena ngati akucitila cinthu cabwino, uyenela kumwetulila kwambili

Kulikonse kumene ungakhale komanso pamene ucita ciliconse, Nthawi Zonse uzikumbukila kukamba “Zikomo!”

ZOCITA

Muŵelengeleni mwana wanu:

1 Atesalonika 5:18

Uzani mwana wanu kuti aloze:

Mphatso Mnyamata

Citseko Cakudya

Pezani zinthu zobisika.

Apulo Telefoni

M’funseni mwana wanu:

N’cifukwa ciani n’cinthu cabwino kukamba “Zikomo”?

[Cithunzi 12]

[Cithunzi 13]

[Cithunzi 13]

[Cithunzi 13]

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani