LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 146 tsa. 11
  • Munacitila Ine

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Munacitila Ine
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Munacitila Ine
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pemphelo la Munthu Wovutika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pemphero la Munthu Wovutika
    Imbirani Yehova
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 146 tsa. 11

Nyimbo 146

Munacitila Ine

Yopulinta

(Mateyu 25:34-40)

  1. Abale a Yesu

    ndi a Nkhosa zina,

    Amatumikila mogwilizana.

    Zimene a nkhosa zina amacita

    Yesu Khristu adzazikumbukila.

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, powatonthoza.

    Zonse zimene munawacitila,

    imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munawacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

  2. “Ninali na njala, ninali na njota,

    Munabwela msanga kunithandiza.”

    “Tiuzeni, izi

    tinacita liti?”

    Ndiyeno Mfumu idzayankha kuti:

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, powatonthoza.

    Zonse zimene munawacitila,

    imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munawacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

  3. “Mokhulupilika munagwila nchito

    yolalikila na abale anga.

    Landilani dziko

    na moyo wosatha.”

    Mfumu idzauza a nkhosa zina.

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, powatonthoza.

    Zonse zimene munawacitila,

    imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munawacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

(Onaninso Miy. 19:17; Mat. 10:40-42; 2 Tim. 1:16, 17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani