LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 26
  • Munacitila Ine

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Munacitila Ine
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Munacitila Ine
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Pemphelo la Munthu Wovutika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pemphero la Munthu Wovutika
    Imbirani Yehova
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 26

NYIMBO 26

Munacitila Ine

Yopulinta

(Mateyu 25:34-40)

  1. 1. Abale a Yesu

    ndi a nkhosa zina,

    Amatumikila mogwilizana.

    Zimene a nkhosa zina amacita

    Yesu Khristu adzazikumbukila.

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, poŵatonthoza.

    Zonse zimene munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

  2. 2. “Ninali na njala, ninali na njota,

    munabwela msanga munathandiza.”

    “Tiuzeni, izi

    tinacita liti?”

    Ndiyeno Mfumu idzayankha kuti:

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, poŵatonthoza.

    Zonse zimene munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

  3. 3. “Mokhulupilika munagwila nchito,

    yolalikila na abale anga.

    Landilani dziko

    na moyo wosatha.”

    Mfumu idzauza a nkhosa zina.

    (KOLASI)

    “Munanitonthoza, poŵatonthoza.

    Zonse zimene munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.

    Zonse imwe munaŵacitila,

    Imwe munali kucitila ine.”

(Onaninso Miy. 19:17; Mat. 10:40-42; 2 Tim. 1:16, 17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani