LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 149 tsa. 14
  • Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cimwemwe Cathu Camuyaya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 149 tsa. 14

Nyimbo 149

Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo

Yopulinta

(Luka 22:20)

  1. Atate Yehova

    tikuyamikani

    cifukwa ca cikondi

    munationetsa.

    Munapeleka mphatso

    ya Mwana wanu

    kuti ise tikapeze

    moyo wosatha.

    (KOLASI)

    Anafela anthu onse

    kuti atipulumutse.

    Ise tidzakuyamikilani

    kwamuyaya.

  2. Mwa cikondi

    Yesu anadzipeleka

    Kufela anthu onse

    akapeze moyo.

    Mphatso imene Yesu

    anapeleka

    imapatsa anthu onse

    ciyembekezo.

    (KOLASI)

    Anafela anthu onse

    kuti atipulumutse.

    Ise tidzakuyamikilani

    kwamuyaya.

(Onaninso Aheb. 9:13, 14; 1 Pet.1:18, 19.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani