LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 154 tsa. 20
  • Tidzapilila Mosalekeza

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tidzapilila Mosalekeza
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Tidzapilila Mosalekeza
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tengelani Citsanzo ca Yehova pa Kupilila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Pirirani Mpaka pa Mapeto
    Imbirani Yehova
  • Pilila Mpaka Mapeto
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 154 tsa. 20

Nyimbo 154

Tidzapilila Mosalekeza

Yopulinta

Daunilodi

  • Mau Cabe

(Mateyu 24:13)

  1. Yesu anati,

    ‘Pililani mayeselo.’

    Anapeleka

    citsanzo ca kupilila.

    Anali kudziŵa

    lonjezo la M’lungu.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

  2. Tingakumane

    Na mavuto nthawi zina.

    Koma tidziŵa

    M’lungu adzatidalitsa

    Na moyo wosatha

    m’dziko la mtendele.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

  3. Sitidzafoka

    Kapena kucita mantha.

    Tidzapilila

    potumikila Yehova.

    Mavuto adzatha

    m’dziko latsopano.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

(Onaninso Mac 20:19, 20; Yak 1:12; 1 Pet 4:12-14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani