LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 129
  • Tidzapilila Mosalekeza

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tidzapilila Mosalekeza
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tidzapilila Mosalekeza
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tengelani Citsanzo ca Yehova pa Kupilila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Pirirani Mpaka pa Mapeto
    Imbirani Yehova
  • Pilila Mpaka Mapeto
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 129

NYIMBO 129

Tidzapilila Mosalekeza

Yopulinta

(Mateyu 24:13)

  1. 1. Yesu anati,

    ‘Pililani mayeselo.’

    Anapeleka

    citsanzo ca kupilila.

    Anali kudziŵa

    lonjezo la M’lungu.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

  2. 2. Tingakumane

    Na mavuto nthawi zina.

    Koma tidziŵa

    M’lungu adzatidalitsa,

    Na moyo wosatha

    m’dziko la mtendele.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

  3. 3. Sitidzafo’ka

    Kapena kucita mantha.

    Tidzapilila

    potumikila Yehova.

    Mavuto adzatha

    m’dziko latsopano.

    (KOLASI)

    Tiyeni tipilile.

    Tikhale olimba.

    Mwa mphamvu ya Yehova,

    Ise tipilile mosaleka.

(Onaninso Mac 20:19, 20; Yak 1:12; 1 Pet 4:12-14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani