LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 12-13
  • Mawu Oyamba a Cigawo 2

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 2
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Cigumula ca Nowa—Ndani Anamvetsela? Ndani Sanamvetsele?
    Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Kutengapo Phunzilo pa Zimene Zinacitika Kumbuyo
    Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
  • Mwana Wabwino, Ndi Mwana Woipa
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Kukwiya Mpaka Kupha Munthu
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 12-13
Nowa aloŵetsa vinyama mu cingalawa

Mawu Oyamba a Cigawo 2

N’cifukwa ciani Yehova anabweletsa cigumula cimene cinawononga anthu m’nthawi yakale? Kuciyambi kwa mbili ya anthu, Satana anapandukila Yehova. Anthu ena monga Adamu, Hava, na mwana wawo Kaini, anasankha kukhala ku mbali yoipa ya Satana. Koma anthu ena ocepa, monga Abele na Nowa, anasankha kukhala ku mbali yabwino ya Yehova. Anthu ambili anakhala oipa kwambili, cakuti Yehova anaŵawononga onse. Cigawo cino, cidzatithandiza kudziŵa kuti Yehova amaona mbali imene tasankha. Ndipo sadzalola anthu oipa kugonjetsa anthu abwino.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Tiyenela kukhala amtendele, osati aciwawa monga Mdyelekezi na atumiki ake

  • Ngati timvetsela kwa Mulungu na kucita zimene afuna monga mmene Nowa anacitila, tidzakhala acimwemwe kwamuyaya

  • Yehova amaona zonse zimene timacita. Zinthu zabwino zimam’kondweletsa, koma zinthu zoipa zimam’khumudwitsa

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani