LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 22-23
  • Mawu Oyamba a Cigawo 3

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 3
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Anamucha kuti “Bwenzi Langa”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Mukhoza Kukhala Bwenzi la Yehova
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Yehova Ndi Bwenzi Lathu Lapamtima
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Abulahamu na Sara Anamvela Mulungu
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 22-23
Abulahamu afotokozela wacicepele Isaki za nyenyezi

Mawu Oyamba a Cigawo 3

Pambuyo pa Cigumula, Baibo imangochula anthu ocepa amene anatumikila Yehova. Mmodzi wa iwo ni Abulahamu, amene anadziŵika monga bwenzi la Yehova. Koma n’cifukwa ciani anachedwa bwenzi la Yehova? Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kudziŵa kuti Yehova amam’konda, na kuti amafuna kum’thandiza. Monga mmene anacitila Abulahamu, komanso amuna ena okhulupilika, monga Loti na Yakobo, na ise tingapemphe thandizo kwa Yehova momasuka. Tingakhale na cidalilo cakuti Yehova adzacita zonse zimene walonjeza.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Citani zilizonse zimene Yehova wakuuzani, olo zikhale zovuta

  • Kukhala pa ubwenzi wabwino na Mulungu ndiye cinthu cofunika ngako kuposa cina ciliconse

  • Yehova amafuna kuti tizikhululukila ena, na kukhazikitsa mtendele mwamsanga

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani