LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 122-123
  • Mawu Oyamba a Cigawo 9

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 9
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Yehoyada Anali Wolimba Mtima
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kamtsikana Kathandiza Mkulu wa Asilikali
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • N’cifukwa Ciyani Tiyenela Kumuopa Yehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Acinyamata—Kodi Mudzakhala na Tsogolo Lotani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 122-123
Kamtsikana kaciisiraeli kakamba na mkazi wa Namani wakhate

Mawu Oyamba a Cigawo 9

M’cigawo cino tidzaphunzila za acicepele, aneneli, komanso mafumu amene anaonetsa cikhulupililo camphamvu mwa Yehova. Ku Siriya, kunali kamtsikana kena kaciisiraeli komwe kanali kukhulupilila kuti mneneli wa Yehova angacilitse Namani. Mneneli Elisa anali na cidalilo conse mwa Yehova kuti adzam’teteza ku gulu la adani ake. Mkulu wa Ansembe Yehoyada anaika moyo wake paciswe, kuti ateteze wacicepele Yehoasi kwa ambuye ake aakazi oipa kwambili, Ataliya. Mfumu Hezekiya inali na cidalilo cakuti Yehova adzapulumutsa Yerusalemu, ndipo iye sanagonje kwa Asuri pomuwopseza. Mfumu Yosiya inafafaniza kulambila mafano m’dziko lawo, inamanganso kacisi, na kuthandiza anthu kuyambanso kulambila koona.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Kucitila umboni za Yehova kulibe kuti ndiwe mwana

  • Tikacita zoyenela, Yehova analonjeza kuti adzakhala nafe

  • Mofanana na Yona, phunzilani kutsatila malangizo a Yehova, ndipo musadandaule ngati zinthu sizinayende mmene munali kufunila

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani