LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 70
  • Funa-funani Oyenelela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Funa-funani Oyenelela
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Fufuzani Anthu Oyenerera
    Imbirani Yehova
  • Mulungu Wamkulu, Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Funani-funani Yehova, Kuti Mukhalebe na Moyo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 70

NYIMBO 70

Funa-funani Oyenelela

Yopulinta

(Mateyu 10:11-15)

  1. 1. Yesu analalikila mwakhama;

    Anaphunzitsa co’nadi.

    Anali kufufuza oyenela,

    Kuti amvetsele uthenga.

    Mwakuŵapatsa moni eninyumba,

    Angamasuke na kumvela.

    Koma ngati akana kumvetsela

    Musaŵatsutse, muŵaleke.

  2. 2. Onse amene akulandilani

    Amalandilanso Yesu.

    Iwo adzapeza moyo wosatha

    Ngati amvetsela uthenga.

    Yehova adzakuuzani zonse

    Zofunika kuti mukambe.

    Mau anu akakhala okoma

    Ofatsa adzakumvelani.

(Onaninso Mac. 13:48; 16:14; Akol. 4:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani