LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 96
  • Fufuzani Anthu Oyenerera

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fufuzani Anthu Oyenerera
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Funa-funani Oyenelela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Wamkulu, Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
    Imbirani Yehova
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Imbirani Yehova
sn nyimbo 96

Nyimbo 96

Fufuzani Anthu Oyenerera

(Mateyu 10:11-15)

1. Ambuye wathu anatisonyeza

Njira yolalikirira:

‘Kulikonse kumene mungapite

Fufuzani oyenerera.

Muziwapatsa moni eni nyumba

Ndikuwafunira mtendere.

Ngati akana sansani fumbi

Kumapazi anu muwasiye.’

2. Onse amene akulandirani

Alandiranso Ambuye.

Mulungu adzawathandizadi

Kuti nawonso atumikire.

Musade nkhawa kuti munenanji,

Yehova adzakuuzani.

Ngati mutayankha mokoma mtima

Ofatsa adzakumverani.

(Onaninso Mac. 13:48; 16:14; Akol. 4:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani