LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 125
  • ‘Acifundo ni Acimwemwe!’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Acifundo ni Acimwemwe!’
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
  • Timatumikila Mulungu “Wacifundo Coculuka”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 125

NYIMBO 125

‘Acifundo ni Acimwemwe!’

Yopulinta

(Mateyu 5:7)

  1. 1. Yehova ni wacifundo,

    Ndipo ni wokoma mtima.

    Iye amasamalila

    Zonse zimene tifuna.

    Ocimwa ngati alapa,

    Amaŵakhululukila.

    Cifukwa iye adziŵa

    Kuti ‘se ndise ofooka.

  2. 2. Tikakhala na cifundo,

    M’lungu adzatidalitsa.

    Adzatikhululukila

    Ise pamene tilakwa.

    Yesu anatiphunzitsa

    Kufunika kwa cifundo.

    Tidzakhala na mtendele,

    Ngati timakhululuka.

  3. 3. Pamene tipatsa ena

    Mphatso zathu za cifundo.

    Ise tisadzitamande,

    Tikhale odzicepetsa.

    Anthu onse acifundo,

    Amakhala acimwemwe.

    Yehova amaŵakonda,

    Iye amaŵadalitsa.

(Onaninso Mat. 6:2-4, 12-14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani