LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm18 masa. 3-4
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
  • Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela wa 2017-2018—Wa Woimila Nthambi
  • Nkhani Zofanana
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Cikondi na Cilungamo Mumpingo Wacikhristu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • “Musaleme pa Kukwanilitsa Cilamulo ca Khristu!”
    Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela wa 2017-2018—Wa Woimila Nthambi
Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela wa 2017-2018—Wa Woimila Nthambi
CA-brpgm18 masa. 3-4

Pezani Mayankho pa Mafunso Aya:

  1. Kodi “cilamulo ca Khristu” n’ciani? (Agal. 6:2)

  2. Kodi tingakwanilitse bwanji cilamulo ca Khristu pamene ena sakutiona? (1 Akor. 10:31)

  3. Kodi timakwanilitsa bwanji cilamulo ca Khristu mu ulaliki? (Luka 16:10; Mat. 22:39; Mac. 20:35)

  4. Kodi cilamulo ca Khristu cimapambana bwanji Cilamulo ca Mose? (1 Pet. 2:16)

  5. Kodi okwatilana ndi makolo angakwanilitse bwanji cilamulo ca Khristu m’banja lawo? (Aef. 5:22, 23, 25; Aheb. 5:13, 14)

  6. Kodi mungakwanilitse bwanji cilamulo ca Khristu ku sukulu? (Sal. 1:1-3; Yoh. 17:14)

  7. Kodi tingawakonde bwanji anthu ena mmene Yesu anakondela ife? (Agal. 6:1-5, 10)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani