LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 160
  • “Uthenga Wabwino”!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Uthenga Wabwino”!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Ya Kaamba ka Mwana Wake Wodzozedwayo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Uthenga Wabwino Umalalikidwa Motani?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 160

NYIMBO 160

“Uthenga Wabwino”!

Yopulinta

(Luka 2:10)

  1. 1. “Ulemelelo kwa Ya”—

    Yesu wabadwa—

    Iye ni mpulumutsi wathu.

    Adzamasula,

    Cilengedwe conse!

    (KOLASI)

    Yesu wabadwa—

    Tonse tikondwe—

    Tiuze onse!

    Yesu ni njila—

    Iye n’co’nadi.

    Onse adziŵe—

    Iye ndiye moyo.

  2. 2. Khristu adzabweletsa.

    Mtendele m’dziko.

    Iye ni njila ya ku moyo.

    Ufumu wake.

    Ulibe mapeto.

    (KOLASI)

    Yesu wabadwa—

    Tonse tikondwe—

    Tiuze onse!

    Yesu ni njila—

    Iye n’co’nadi.

    Onse adziŵe—

    Iye ndiye moyo.

    (KOLASI)

    Yesu wabadwa—

    Tonse tikondwe—

    Tiuze onse!

    Yesu ni njila—

    Iye n’co’nadi.

    Onse adziŵe—

    Iye ndiye moyo.

(Onaninso Mat. 24:14; Yoh. 8:12; 14:6; Yes. 32:1; 61:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani