LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

Nsanja ya Mlonda May-June

“Anthu ambili masiku ano sadziŵa kuti Baibulo lili ndi mayankho okhutilitsa a mafunso ngati awa. [Muonetseni mafunso ali kuciyambi kwa nkhani yoyamba m’magazini a Nsanja ya Mlonda ndi kuŵelenga naye 2 Timoteyo 3:16] Magazini iyi ifotokoza mmene mungapezele mayankho m’Baibulo lanu.”

Galamukani! June

“Tonsefe timavutika ndi matenda. Conco tikuceza ndi anzathu mwacidule kuti tikambilane nao vesi lolimbikitsa ili la m’Baibulo. [Ŵelengani Yesaya 33:24a.] Zikanakhala kuti sitidwala, kodi muganiza kuti moyo ukanakhala bwanji? [Yembekezani ayankhe.] Poyembekezela kuti ulosiwu udzakwanilitsidwe, pali zinthu 5 zimene zingatithandize kukhala ndi thanzi labwino. Magazini iyi ifotokoza zinthu zimenezo.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani