LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsa. 4
  • Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Acicepele—Kodi Mukukula Mwauzimu?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabala Zipatso mwa Kupilila’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Muziona Okalamba Okhulupilika Kuti ni Ofunika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 August tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 92-101

Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba

Wacinyamata ndi wacikulile ayendela pamodzi pafupi ndi mtengo wa kanjedza

92:12

Mitengo ina ya kanjedza imakhala zaka zoposa 100, ndipo imabalabe zipatso

Acikulile amabala zipatso zauzimu mwa . . .

92:13-15

  • kupemphelela ena

  • kuphunzila Baibulo

  • kupezeka pamisonkhano na kuyankhapo

  • kuuzako ena zinthu zimene adziŵa

  • kulalikila modzipeleka

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani