LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 June tsa. 5
  • Acicepele—Kodi Mukukula Mwauzimu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Acicepele—Kodi Mukukula Mwauzimu?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Ndimwe Munthu Wakuthupi Kapena Wauzimu?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kalamilani Nchito Yabwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Amabala Zipatso Ngakhale ni Okalamba
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 June tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 2-3

Acicepele—Kodi Mukukula Mwauzimu?

Kungoyambila ali mwana, Yesu anapeleka citsanzo cabwino kwambili pa nkhani yotumikila Yehova na kulemekeza makolo ake.

Acicepele, kodi mungatengele bwanji citsanzo ca Yesu m’mbali zotsatilazi?

  • 2:41, 42

    Yesu wacicepele na a m’banja lake akupita ku Yerusalemu kukacita cikondwelelo ca Pasika

    kutengako mbali m’zocitika zauzimu:

  • 2:46, 47

    Yesu ali na zaka 12, ali na aphunzitsi pa kacisi

    kuwonjezela cidziŵitso:

  • 2:51, 52

    Yesu akuwaonetsa ulemu makolo ake

    kulemekeza makolo anu:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani