LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 November tsa. 4
  • Muzikondwela Pogwila Nchito Mwakhama

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzikondwela Pogwila Nchito Mwakhama
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Sangalalani Cifukwa Cogwila Nchito Yanu Mwakhama
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
  • Muzikondwela Nayo Nchito Yanu
    Mmene Tingakhalilebe mu Cikondi ca Mulungu
  • Mungacite Ciani Kuti Muzisangalala Ngati Mumagwila Nchito Yolimba?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Kodi Kugwila Nchito Mwamphamvu N’kofunikadi?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 November tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MLALIKI 1–6

Muzikondwela Pogwila Nchito Mwakhama

Yehova amafuna kuti tizikondwela na nchito yathu, ndipo amatiuza zimene zingatithandize. Munthu angayambe kukondwela na nchito yake ngati amaiona moyenela.

Kuti muzikondwela na nchito yanu, mufunika . . .

3:13; 4:6

  • Mwamuna akondwela pogwila nchito yake

    kukhala na maganizo oyenela

  • Mwamuna aganizila mmene nchito yake imapindulitsila ena

    kuganizila mmene nchito yanu imapindulitsila ena

  • Mwamuna na banja lake afuna kudya cakudya

    kugwila nchito mwakhama. Koma mukakomboka, muzikhala na nthawi yoceza na banja lanu ndi kucita zinthu zauzimu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani