LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 April tsa. 3
  • Lolani Kuti Yehova Aumbe Maganizo na Khalidwe Lanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lolani Kuti Yehova Aumbe Maganizo na Khalidwe Lanu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Amatiumba
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Kodi Mumalola Kuti Woumba Wamkulu Akuumbeni?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 April tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 17-21

Lolani Kuti Yehova Aumbe Maganizo na Khalidwe Lanu

Woumba aumba ciwiya ca dothi

Lolani Kuti Yehova Akuumbeni

18:1-11

  • Yehova amaumba makhalidwe athu a kuuzimu mwa kutipatsa uphungu ndi kutilanga

  • Tifunika kukhala ofeŵa ndi omvela

  • Yehova satikakamiza kucita zimene sitifuna

Woumba angasinthe maganizo ake a moseŵenzetsela cimene waumba

  • Popeza Yehova anatipatsa ufulu wosankha zocita, tingasankhe kumulola kutiumba kapena kukana

  • Yehova amasintha mocitila ndi anthu malinga na mmene amalabadilila malangizo ake

    Citsanzo coonetsa mmene Woumba Wamkulu amatiumbila, m’bale akucoka pali akulu mokwiya ndiyeno abwelelanso ndi kukambilana nawo

Kodi ine nifuna kuti Yehova aniumbe pambali ziti?

KODI MUDZIŴA?

Zidutswa zophwanyika za dothi pafupi na mbiya

Kuseŵenzetsa dongo, kapena kuti dothi loumbila, kunali kofala m’nthawi za m’Baibo. Dongo lonyowa ndi lofeŵa bwino, silivuta kuumbila cinthu, ndi kulembapo zimene ufuna. Koma dothi ni dothi, olo aliwoche bwanji m’moto, kulimba kwake n’kwapang’ono.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani