LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 April tsa. 7
  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Atumiza Yeremiya Kuti Akalalikile
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yeremiya Sanaleke Kulankhula za Yehova
    Phunzitsani Ana Anu
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 April tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 25-28

Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya

Mneneli Yeremiya anacenjeza kuti Yerusalemu adzasakazidwa

Yeremiya anacenjeza kuti Yerusalemu adzasakazidwa mofanana ndi mzinda wa Silo

26:6

  • Pa nthawi ina likasa la pangano, loimila Yehova, linali kusungidwila ku Silo

  • Yehova analola kuti Afilisiti alande likasalo, ndipo siinabwelelenso ku Silo

Ansembe, aneneli, akugwila mneneli Yeremiya

Ansembe, aneneli, ndi anthu onse anaopseza kuti adzamupha Yeremiya

26:8, 9, 12, 13

  • Anthu anam’gwila Yeremiya cifukwa colosela zakuti kacisi adzawonongedwa

  • Yeremiya sanaope ndi kuthaŵa

Yeremiya mneneli

Yehova anam’teteza Yeremiya

26:16, 24

  • Yeremiya anakhalabe wolimba mtima, ndipo Yehova sanamusiye

  • Mulungu anacititsa Ahikamu wolimba mtima kuteteza Yeremiya

Yeremiya sanaleke kulengeza uthenga umene anthu anali kukwiya nawo cifukwa Yehova anali kumucilikiza na kumulimbikitsa kwa zaka 40

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani