LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsa. 2
  • Funani Yehova Tsiku la Mkwiyo Wake Lisanafike

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Funani Yehova Tsiku la Mkwiyo Wake Lisanafike
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Zefaniya
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Mukondweletse Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 December tsa. 2
Zefaniya akamba na Aisiraeli

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | ZEFANIYA 1-HAGAI 2

Funani Yehova Tsiku la Mkwiyo Wake Lisanafike

Zef. 2:2, 3

Kuti Yehova akatibise pa tsiku la mkwiyo wake, kudzipeleka cabe kwa iye sikokwanila. Tifunikanso kumvela malangizo amene Zefaniya anapeleka kwa Aisiraeli.

  • Funani Yehova: Limbitsani ubwenzi wanu na Yehova mwa kugwilizana kwambili na gulu lake

  • Funani cilungamo: Muzitsatila miyezo yolungama ya Yehova

  • Funani cifatso: Modzicepetsa, muzicita cifunilo ca Mulungu ndi kumalandila uphungu

Ningacite ciani kuti niwonjezele kufuna-funa Yehova, cilungamo cake, na cifatso?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani