LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsa. 3
  • Pitani Mukapange Ophunzila—Cifukwa ciani, Kuti, ndipo Motani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitani Mukapange Ophunzila—Cifukwa ciani, Kuti, ndipo Motani?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tingathandizile Ena Kusunga Malamulo a Khristu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Kodi Tingaphunzile Ciani pa Zovala za Ansembe?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 April tsa. 3
Yesu alamula otsatila ake kukapanga ophunzila

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 27-28

Pitani Mukapange Ophunzila—Cifukwa ciani, Kuti, ndipo Motani?

28:18-20

Cifukwa ciani? Yesu analandila ulamulilo waukulu kucokela kwa Yehova.

Kuti? Yesu analamula otsatila ake kupanga ophunzila pakati pa “anthu a mitundu yonse”

Kuphunzitsa ena kusunga zinthu zonse zimene Yesu anatilamula ni nchito yofunika kupitiliza

  • Atsogoza phunzilo la Baibo

    Kodi anthu ena tingawaphunzitse bwanji malamulo a Yesu?

  • Athandiza wophunzila Baibo kuseŵenzetsa zimene Yesu anaphunzitsa

    Tingawathandize bwanji ophunzila athu kuseŵenzetsa zimene Yesu anaphunzitsa?

  • Ali na wophunzila Baibo mu ulaliki

    Tingawathandize bwanji ophunzila athu kutengela citsanzo ca Yesu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani