LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 June tsa. 4
  • Tengelani Kudzicepetsa kwa Mariya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tengelani Kudzicepetsa kwa Mariya
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Gabirieli Aonekela kwa Mariya
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mngelo Acezela Mariya
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 June tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 1

Tengelani Kudzicepetsa kwa Mariya

Yehova anapatsa Mariya mwayi wapadela cifukwa anali na mtima wabwino.

Mngelo Gabirieli akukamba na Mariya

1:38, 46-55

Kodi mau amene Mariya anakamba aonetsa bwanji kuti anali . . .

  • wodzicepetsa?

  • wa cikhulupililo colimba?

  • kuwadziŵa bwino Malemba?

  • munthu woyamikila?

MAFUNSO OFUNIKA KUWASINKHASINKHA

Kodi nimakhulupilila na mtima wonse kuti Yehova adzanicitila zinthu mogwilizana na cifunilo cake? Ningatengele bwanji citsanzo ca Mariya?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani