LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsa. 4
  • Fanizo la Msamariya Wacifundo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fanizo la Msamariya Wacifundo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Fanizo la Mwana Woloŵelela
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Phunzilamponi Kanthu pa Fanizo la Ndalama 10 za Mina
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 July tsa. 4
Msamaliya wabwino amanga zilonda za Myuda wovulazidwa

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 10-11

Fanizo la Msamariya Wacifundo

10:25-37

Yesu anapeleka fanizo ili pofuna kuyankha funso lakuti, “Mnzanga amene ndikuyenela kumukonda ndani kwenikweni?” (Luka 10:25-29) Iye anadziŵa kuti m’kupita kwa nthawi, mpingo wacikhristu udzakhala na anthu “osiyana-siyana”—Asamariya, na anthu amitundu ina. (Yoh. 12:32) Fanizo limeneli linaphunzitsa otsatila ake kuti afunika kuyesetsa kukonda anthu, ngakhale amene aoneka kuti ni osiyana nawo kwambili.

Anthu a mitundu yosiyana-siyana aceza na kudyela pamodzi

DZIFUNSENI KUTI:

  • Kodi nimawaona bwanji abale na alongo a mitundu ina?

  • Kodi nimakonda ngako kuceza na anthu amene nimafanana nawo?

  • Kodi ningafutukule mtima wanga mwa kudziŵana bwino na Akhristu anzanga a mitundu ina? (2 Akor. 6:13)

Nifuna nikapemphe kuti . . .

  • nikapite naye mu ulaliki

  • akabwele ku nyumba kwathu ku cakudya

  • tikacitile pamodzi Kulambila kwa Pabanja kotsatila

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani