LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsa. 6
  • Fanizo la Mwana Woloŵelela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fanizo la Mwana Woloŵelela
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Fanizo la Msamariya Wacifundo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Muzikhala Okonzeka Kukhululukila Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Phunzilamponi Kanthu pa Fanizo la Ndalama 10 za Mina
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 July tsa. 6
Tate alandila mwana wake amene analoŵelela

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 14-16

Fanizo la Mwana Woloŵelela

15:11-32

Zimene tiphunzilapo pa fanizo ili.

  • Cimakhala canzelu kukhalabe m’gulu lotetezeka la anthu a Mulungu, limene Atate wathu wacikondi akulisamalila

  • Tikapatuka pa njila ya Yehova, modzicepetsa tiyenela kubwelelanso tili na cidalilo cakuti Yehova adzatikhululukila

  • Tingatengele citsanzo ca Yehova mwa kulandila na manja aŵili anthu amene alapa na kubwelelela mu mpingo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani