LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 August tsa. 2
  • Muzionetsa Kuyamikila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzionetsa Kuyamikila
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Cikumbutso Cimene Cikubwela Cidzatipatsa Mwai Woyamikila
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • “Yehova Ndidzamubwezela Ciani?”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • N’cifukwa Ciani Tiyenela Kuonetsa Kuyamikila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 August tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 17-18

Muzionetsa Kuyamikila

17:11-18

Amuna 10 akhate apempha Yesu kuti awacitile cifundo, acilitsidwa, koma mmodzi cabe ndiye akuyamikila Yesu

Kodi cocitika ici citiphunzitsa ciani pa nkhani ya kuyamikila?

  • Ciyamikilo cathu sicifunika cabe kuthela mu mtima koma tifunika kuciwonetsa

  • Kukamba mau oyamikila mocokela pansi pa mtima kumaonetsa kuti tili na cikondi cacikhristu, ndipo ni cizindikilo cakuti tili na aulemu

  • Amene amafuna kukondweletsa Khristu ali na udindo kwa anthu onse, wowaonetsa cikondi na kuwayamikila, mosasamala kanthu za dziko lawo, mtundu wawo kapena cipembedzo cawo.

Ni liti pamene n’nayamikilako munthu amene ananithandiza?

Ni liti pamene n’nalembelako munthu kameseji kapena kakalata komuyamikila?

Mlongo akulemba kakalata ka ciyamikilo
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani