LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsa. 7
  • “Yehova Ndidzamubwezela Ciani?”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Yehova Ndidzamubwezela Ciani?”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Cikumbutso Cimene Cikubwela Cidzatipatsa Mwai Woyamikila
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Muzionetsa Kuyamikila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Mulungu Akuonetsa Cikondi Cake Kwa Ife”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 August tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 110–118

“Yehova Ndidzamubwezela Ciani?”

Wamasalimo aliza zeze
Manja a munthu omangidwa na cingwe

Wamasalimo anayamikila kwambili Yehova cifukwa anamupulumutsa ku “zingwe za imfa.” (Sal. 116:3) Iye anali wofunitsitsa kuonetsa kuti amayamikila Yehova mwa kusunga malonjezo ake onse ndi kum’tumikila modzipeleka.

N’zinthu ziti zimene Yehova wanicitila mlungu uno kuti nimuyamikile?

Ningaonetse bwanji kuti namuyamikila Yehova?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani