LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsa. 3
  • Tengelani Cifundo ca Yesu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tengelani Cifundo ca Yesu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Tengelani Khalidwe la Yehova la Cifundo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Muzicitila Cifundo Anthu “Kaya Akhale a Mtundu Wotani”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Onetsani Cifundo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Muzimvelela Ena Cifundo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 October tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 11-12

Tengelani Cifundo ca Yesu

Yesu alila pamene Marita akumuuza kuti Lazaro wamwalila

11:23-26, 33-35, 43, 44

N’cifukwa ciani cifundo ca Yesu na kukoma mtima kwake kunali kocititsa cidwi?

  • Ngakhale kuti Yesu sanakumane na mavuto onse amene anthu ena anapitamo, iye anali kumvetsetsa mmene iwo anali kumvelela

  • Sanali kucita manyazi kuonetsa poyela mmene anali kumvelela

  • Sanali kulekelela koma anali kuthandiza

Mlongo wacikulile wagwilila mlongo wacicepele ndipo akumutonthoza

Ningaonetse bwanji kuti nimaganizila anthu ena?

Ningathandize bwanji ofunikila thandizo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani