LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 4
  • Anapitiliza Kulankhula Mawu a Mulungu Molimba Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Anapitiliza Kulankhula Mawu a Mulungu Molimba Mtima
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Yesu Anali Kukonda Anthu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 4
Petulo na Yohane akukamba molimba mtima kwa mkulu wa ansembe na anthu ena

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 4-5

Anapitiliza Kulankhula Mawu a Mulungu Molimba Mtima

4:5-13, 18-20, 23-31

N’ciani cinathandiza atumwi kukhala aphunzitsi oyenelela? N’ciani cinawathandiza kukamba mwa cidalilo komanso molimba mtima? Iwo “anali kuyenda ndi Yesu,” Mphunzitsi Waluso, ndipo anaphuzila kwa iye. (Mac. 4:13) Kodi tingaphunzile zotani kwa Yesu zimene zingatithandize kukhala aphunzitsi a Baibo aluso?

Gwilizanitsani malemba otsatilawa na phunzilo lake.

MALEMBA

PHUNZILO

  • Mat. 6:33; Maliko 6:31-34

  • Mat. 10:18-20; 21:23-27

  • Mat. 21:15, 16; Yoh. 7:16

  • Mat. 21:22; Luka 22:39-41

  • Tizidalila Yehova

  • Tiziphunzitsa zogwilizana na Malemba

  • Tisamaope anthu

  • Tiziika utumiki patsogolo pa zofuna zathu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani