LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 6
  • Paulo Apita ku Roma

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Paulo Apita ku Roma
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Paulo Atumizidwa ku Roma
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Limbani Mtima—Yehova Ndiye Mthandizi Wanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Pitani Mukapange Ophunzila—Cifukwa ciani, Kuti, ndipo Motani?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 27-28

Paulo Apita ku Roma

27:23, 24; 28:1, 2, 16, 17

Paulo sanaleke kulalikila ena ngakhale kuti anali mkaidi. Pamene iye anali m’ngalawa, analalikila anthu oyendetsa ngalawayo komanso amene anali naye paulendowo. Ngalawa itasweka pa cilumba ca Melita, mosakayikila iye anatengelapo mwayi wolalikila anthu amene anawacilitsa. Pambuyo pa masiku atatu Paulo atafika ku Roma, anaitana amuna olemekezeka pakati pa Ayuda kuti awalalikile. Pa zaka ziŵili zimene iye anali pa ukaidi wa pa nyumba, analalikila onse obwela kudzamuona.

Mungacite ciani kuti muzilalikila uthenga wabwino olo kuti muli na zopinga?

Paulo alalikila amuna olemekezeka aciyuda ku Roma pamene ali womangidwa unyolo kwa msilikali; Njila imene Paulo anadzela pocoka ku Kaisareya kupita ku Roma
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani