LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsa. 3
  • Utumiki Wathu Wothandiza Pakacitika Tsoka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Utumiki Wathu Wothandiza Pakacitika Tsoka
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Utumiki Wopeleka Thandizo Pakacitika Ngozi
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Kodi Mudzacitako Upainiya Wothandiza m’Mwezi wa March Kapena April?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 May tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 AKORINTO 7-10

Utumiki Wathu Wothandiza Pakacitika Tsoka

8:1-4; 9:7

Akhristufe timacita utumiki wa mbali ziŵili. Mbali yoyamba ni “utumiki wokhazikitsanso mtendele,” kapena kuti nchito yathu yolalikila na kuphunzitsa. Mbali yaciŵili ni “utumiki wothandiza” okhulupilila anzathu. (2 Akor. 5:18-20; 8:4) Conco kuthandiza Akhristu ovutika ni mbali ya utumiki wathu wopatulika. Tikamatengako mbali,

  • timasamalila bwino zofunika za abale na alongo athu. —2 Akor. 9:12a

  • timathandiza Akhristu ovutika kuyambanso kucita zinthu zauzimu, zimene ziphatikizapo kugwila nchito yolalikila modzipeleka monga njila yoonetsela ciyamikilo cawo kwa Yehova.—2 Akor. 9:12b

  • timalemekeza Yehova. (2 Akor. 9:13) Utumiki wathu wothandiza pakacitika tsoka umacitila umboni kwa aliyense, kuphatikizapo anthu amene amaona Mboni za Yehova m’njila yolakwika

Banja m’nthawi za Baibo likupanga copeleka ca ndalama; mlongo akuyang’ana abale a mu Komiti Yothandizila Pakagwa Tsoka pamene akukonza nyumba yake
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani