LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 June tsa. 3
  • Colinga ca Dongosolo la Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Colinga ca Dongosolo la Mulungu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kuyembekezela Moleza Mtima Kumatithandiza Kupilila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • M’kope Ino ya Galamuka!
    Galamuka!—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 June tsa. 3
Mpando wacifumu wa Yehova

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AEFESO 1-3

Colinga ca Dongosolo la Mulungu

1:8-10

Dongosolo la Yehova ni makonzedwe amene iye waika kuti agwilizanitse onse a m’banja lake.

  • Limakonzekeletsa odzozedwa kuti akakhale kumwamba pamodzi na Yesu Khristu, Mutu wawo wauzimu

  • Limakonzekeletsa amene adzakhala padziko lapansi pamene Ufumu wa Mesiya udzayamba kulamulila

Kodi ningalimbikitse mgwilizano m’gulu la Yehova m’njila ziti?

Alongo aŵili osiyana mtundu akuseŵenzela pamodzi mu ulaliki; kamnyamata na atate ŵake apatsa moni m’bale wacikulile m’Nyumba ya Ufumu; mwamuna akumvetsela mkazi wake mwachelu
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani