LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsa. 3
  • “Pitilizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Pitilizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Pitilizani Kulimbikitsana Tsiku na Tsiku’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • “Tiyeni Tilimbikitsane, Ndipo Tiwonjezele Kucita Zimenezi”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Tilimbikitsane Wina na Mnzake
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tizilimbikitsana
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 July tsa. 3
Mlongo wacikulile akupatsa khofi alongo aŵili acitsikana

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 1 ATESALONIKA 1-5

“Pitilizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”

5:11-14

Mkhristu aliyense, angakwanitse kulimbikitsa ena. Mwacitsanzo, timalimbikitsa Akhristu anzathu ngati tipezeka pa misonkhano nthawi zonse, komanso ngati tigwila nawo nchito yolalikila. Mwina timacita zimenezi “movutikila kwambili,” cifukwa ca thanzi lofooka kapena zovuta zina. (1 Ates. 2:2) Kuwonjezela apo, tingakonzekeletu kapena kufufuzilatu kukali nthawi, zinthu zolimbikitsa zimene tingakambe kwa wokhulupilila mnzathu amene afunika cilimbikitso.

N’kuti kumene mungapeze mfundo zolimbikitsila munthu amene wakumana na vuto linalake?

N’ndani amene mungakonde kumulimbikitsa mu mpingo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani