LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 August tsa. 4
  • “Kuika Akulu”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Kuika Akulu”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Dongosolo la Mpingo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Oyang’anila Oweta Nkhosa za Mulungu
    Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
  • Muzionetsa kuti Mumayamikila “Mphatso za Amuna”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 August tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | TITO 1–FILIMONI

“Kuika Akulu”

Tito 1:5-9

Tito akukambilana na abale a mu mpingo wacikhristu woyambilila

Tito anapatsidwa nchito ‘yoika akulu mu mzinda uliwonse.’ Citsanzo ca m’Baibo ici n’cimene timatsatila masiku ano pamene oyang’anila madela amaika akulu mu mipingo.

BUNGWE LOLAMULILA

Potengela citsanzo ca m’nthawi ya atumwi, Bungwe Lolamulila linapatsa oyang’anila madela mphamvu zoika pa udindo akulu na atumiki othandiza.

Zigawo

OYANG’ANILA MADELA

Woyang’anila dela aliyense afunika kupenda mosamala komanso mwa pemphelo, ziyamikilo zimene akulu apanga zokhudza abale. Akatelo, aike pa udindo amuna amene akuyeneleladi.

Zigawo

AKULU

Pamene akulu aikidwa pa udindo, afunika kukhalabe okwanilitsa ziyenelezo za m’Malemba.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani