LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 December tsa. 2
  • Khamu Lalikulu Losaŵelengeka Likudalitsidwa na Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khamu Lalikulu Losaŵelengeka Likudalitsidwa na Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • “Taonani! “Khamu Lalikulu la Anthu”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Khamu Lalikulu la Nkhosa Zina Litamanda Mulungu na Khristu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Usatsatile Khamu la Anthu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 December tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 7-9

Khamu Lalikulu Losaŵelengeka Likudalitsidwa na Yehova

7:9, 14-17

A khamu lalikulu avala mikanjo yoyela, ndipo anyamula nthambi za kanjedza m’manja mwawo

N’cifukwa ciani Yehova akudalitsa khamu lalikulu?

  • Iwo “akuimilila pamaso pa mpando wacifumu” wa Yehova, mwa kucilikiza ndi mtima wonse ucifumu wake

  • Iwo avala “mikanjo yoyela,” kuonetsa kuti ni oyela, ndiponso kuti akuimilila pamaso pa Yehova mwacilungamo cifukwa ca cikhulupililo cawo mu nsembe ya Khristu

  • Iwo akucita “utumiki wopatulika usana ndi usiku,” mwa kulambila Yehova mosalekeza ndiponso mwakhama

Ningacite ciani kuti nikhale mmodzi wa khamu lalikulu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani